The Lord's Prayer-Chichewa


From the Open Files of:

NW Synod of Wisconsin Resource Center, (715) 833-1153

Contributed by:

Diane Kaufmann, Companion Synod Coordinator, NW Synod of WI

This file is available in
Rich Text Format version for editing


Download this file to print out bookmarks with the Lord's Prayer on each side - one side in English and the other in Chichewa.

 

 

Pemphero la Ambuye

Atate wathu wa kumwamba,
dzina lanu liyeretsedwe,
ufumu wanu udze,
kufuna kwanu kuchitidwe,
monga kumwamba chomwecho pansi pano.

Mutipatse ife lero chakudya chathu chalero,
ndipo mutikhululukire ife machimo athu,
monga ifenso tiwakhululukira otichimwira,
musatitengere ife kokatiyesa,
koma mutipulumutse ife kwa woipayo.

Chifukwa wanu uli ufumu ndi mphamvu ndi
ulemerero wa nthawi zonse.
Amen.


[ MALAWI ] • [ HOME ]

© Copyright 2004 by the Northwest Synod of Wisconsin Resource Center. Please see our usage policy.

NW Synod of Wisconsin Resource Center